Eksodo 10:23 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Palibe amene anatha kuona mnzake kapena kuchoka pa khomo pake kwa masiku atatu. Koma kumalo kumene kumakhala Aisraeli kunali kowala. Onani mutuwoBuku Lopatulika23 sanaonane, sanaukenso munthu pamalo pake, masiku atatu; koma kwa ana onse a Israele kudayera m'nyumba zao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 sanaonane, sanaukenso munthu pamalo pake, masiku atatu; koma kwa ana onse a Israele kudayera m'nyumba zao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Aejipitowo sankathanso kuwonana, ndipo palibe ndi mmodzi yemwe amene adachoka pakhomo pake masiku atatu onsewo. Koma Aisraele okha ankakhala koŵala ndithu kuja ankakhalaku. Onani mutuwo |