Eksodo 10:22 - Buku Lopatulika22 Ndipo Mose anatambasulira dzanja lake kuthambo; ndipo munali mdima bii m'dziko lonse la Ejipito masiku atatu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ndipo Mose anatambasulira dzanja lake kuthambo; ndipo munali mdima bii m'dziko lonse la Ejipito masiku atatu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Mose adakweza dzanja lake kumwamba, ndipo pa masiku atatu, mudagwa mdima wandiweyani m'dziko lonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Choncho Mose anakweza dzanja lake kumwamba ndipo mdima wandiweyani unaphimba dziko lonse la Igupto kwa masiku atatu. Onani mutuwo |