Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Danieli 1:21 - Buku Lopatulika

21 Nakhala moyo Daniele mpaka chaka choyamba cha mfumu Kirusi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 Nakhala moyo Daniele mpaka chaka choyamba cha mfumu Kirusi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Ndipo Danieli anali kumeneko mpaka chaka choyamba cha ufumu wa Koresi.

Onani mutuwo Koperani




Danieli 1:21
4 Mawu Ofanana  

Chaka choyamba tsono cha Kirusi mfumu ya ku Persiya, kuti akwaniridwe mau a Yehova m'kamwa mwa Yeremiya, Yehova anautsa mzimu wa Kirusi, kuti abukitse mau mu ufumu wake wonse, nawalembenso, ndi kuti,


Atero Kirusi mfumu ya ku Persiya, Yehova Mulungu Wam'mwamba anandipatsa maufumu onse a padziko lapansi, nandilangiza ndimmangire nyumba mu Yerusalemu, ndiwo mu Yuda.


Chaka chachitatu cha Kirusi mfumu ya Persiya, chinavumbulutsidwa chinthu kwa Daniele, amene anamutcha Belitesazara; ndipo chinthucho nchoona, ndicho nkhondo yaikulu; ndipo anazindikira chinthucho, nadziwa masomphenyawo.


Momwemo Daniele amene anakuzikabe pokhala Dariusi mfumu, ndi pokhala mfumu Kirusi wa ku Persiya.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa