Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Danieli 1:13 - Buku Lopatulika

13 Pamenepo mupenye maonekedwe athu ndi maonekedwe a anyamata akudya chakudya cha mfumu; ndi monga umo muonera, muchitire anyamata anu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Pamenepo mupenye maonekedwe athu ndi maonekedwe a anyamata akudya chakudya cha mfumu; ndi monga umo muonera, muchitire anyamata anu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Ndipo mudzafananize maonekedwe athu ndi a anyamata amene akudya chakudya cha mfumu, ndi kuti mudzachite ndi anyamata anu monga momwe mudzawaonere.”

Onani mutuwo Koperani




Danieli 1:13
2 Mawu Ofanana  

Muyesetu anyamata anu masiku khumi; atipatse zomera m'nthaka tidye, ndi madzi timwe.


Ndipo anawamvera mau awa, nawayesa masiku khumi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa