Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Danieli 1:14 - Buku Lopatulika

14 Ndipo anawamvera mau awa, nawayesa masiku khumi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Ndipo anawamvera mau awa, nawayesa masiku khumi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Choncho anawavomera ndipo anawayesa pa masiku khumi.

Onani mutuwo Koperani




Danieli 1:14
3 Mawu Ofanana  

Pamenepo mupenye maonekedwe athu ndi maonekedwe a anyamata akudya chakudya cha mfumu; ndi monga umo muonera, muchitire anyamata anu.


Atatha masiku khumiwo tsono, anaona kuti maonekedwe ao ndi kunenepa kwao anaposa anyamata onse adadyawo zakudya za mfumu.


Usaope zimene uti udzamve kuwawa; taona, mdierekezi adzaponya ena a inu m'nyumba yandende, kuti mukayesedwe; ndipo mudzakhala nacho chisautso masiku khumi. Khala wokhulupirika kufikira imfa, ndipo ndidzakupatsa iwe korona wa moyo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa