Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Danieli 1:14 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Choncho anawavomera ndipo anawayesa pa masiku khumi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

14 Ndipo anawamvera mau awa, nawayesa masiku khumi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Ndipo anawamvera mau awa, nawayesa masiku khumi.

Onani mutuwo Koperani




Danieli 1:14
3 Mawu Ofanana  

Ndipo mudzafananize maonekedwe athu ndi a anyamata amene akudya chakudya cha mfumu, ndi kuti mudzachite ndi anyamata anu monga momwe mudzawaonere.”


Pakutha pa masiku khumi iwo anaoneka athanzi ndi odya bwino kuposa aliyense wa anyamata amene ankadya chakudya cha mfumu aja.


Musachite mantha ndi zimene muti musauke nazo posachedwapa. Ndithu, Satana adzayika ena a inu mʼndende pofuna kukuyesani, ndipo mudzazunzika kwa masiku khumi. Khalani okhulupirika ngakhale zitafika pa imfa, ndipo Ine ndidzakupatsani chipewa cha ulemerero wamoyo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa