Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Danieli 1:13 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Ndipo mudzafananize maonekedwe athu ndi a anyamata amene akudya chakudya cha mfumu, ndi kuti mudzachite ndi anyamata anu monga momwe mudzawaonere.”

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

13 Pamenepo mupenye maonekedwe athu ndi maonekedwe a anyamata akudya chakudya cha mfumu; ndi monga umo muonera, muchitire anyamata anu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Pamenepo mupenye maonekedwe athu ndi maonekedwe a anyamata akudya chakudya cha mfumu; ndi monga umo muonera, muchitire anyamata anu.

Onani mutuwo Koperani




Danieli 1:13
2 Mawu Ofanana  

“Chonde mutiyese ife akapolo anu pa masiku khumi: mutipatse masamba okha kuti tidye ndi madzi akumwa.


Choncho anawavomera ndipo anawayesa pa masiku khumi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa