Afilipi 2:9 - Buku Lopatulika9 Mwa ichinso Mulungu anamkwezetsa Iye, nampatsa dzina limene liposa maina onse, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Mwa ichinso Mulungu anamkwezetsa Iye, nampatsa dzina limene liposa maina onse, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Chifukwa cha chimenechi Mulungu adamkweza kopambana, nampatsa dzina lopambana dzina lina lililonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Choncho Mulungu anamukweza Iye kukhala wapamwamba kwambiri, ndipo anamupatsa dzina loposa dzina lina lililonse Onani mutuwo |