Afilipi 2:10 - Buku Lopatulika10 kuti m'dzina la Yesu bondo lililonse lipinde, la za m'mwamba ndi za padziko, ndi za pansi padziko, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 kuti m'dzina la Yesu bondo lililonse lipinde, la za m'mwamba ndi za padziko, ndi za pansi pa dziko, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Adachita zimenezi kuti pakumva dzina la Yesu, zolengedwa zonse kumwamba, pansi pano ndi pansi pa dziko, zidzagwade pansi mopembedza, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 kuti pakumva dzina la Yesu, bondo lililonse limugwadire, kumwamba ndi pa dziko lapansi ndi pansi pa dziko, Onani mutuwo |