Afilipi 2:9 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Choncho Mulungu anamukweza Iye kukhala wapamwamba kwambiri, ndipo anamupatsa dzina loposa dzina lina lililonse Onani mutuwoBuku Lopatulika9 Mwa ichinso Mulungu anamkwezetsa Iye, nampatsa dzina limene liposa maina onse, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Mwa ichinso Mulungu anamkwezetsa Iye, nampatsa dzina limene liposa maina onse, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Chifukwa cha chimenechi Mulungu adamkweza kopambana, nampatsa dzina lopambana dzina lina lililonse. Onani mutuwo |
Ulamuliro ndi mtendere wake zidzakhala zopanda malire. Iye adzalamulira ufumu wake ali pa mpando waufumu wa Davide, ndipo adzawukhazikitsa ndi kuwuchirikiza mwa chiweruzo cholungama ndi pochita zachilungamo kuyambira nthawi imeneyo mpaka muyaya. Ndi mtima wake wonse, Yehova Wamphamvuzonse watsimikiza kuchita zimenezi.