Afilipi 2:8 - Buku Lopatulika8 ndipo popezedwa m'maonekedwe ngati munthu, anadzichepetsa yekha, nakhala womvera kufikira imfa, ndiyo imfa ya pamtanda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 ndipo popezedwa m'maonekedwe ngati munthu, anadzichepetsa yekha, nakhala womvera kufikira imfa, ndiyo imfa ya pamtanda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Ali munthu choncho adadzichepetsa, adakhala womvera mpaka imfa, imfa yake yapamtanda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Ndipo pokhala munthu choncho anadzichepetsa yekha ndipo anamvera mpaka imfa yake, imfa yake ya pamtanda! Onani mutuwo |