3 Yohane 1:3 - Buku Lopatulika3 Pakuti ndinakondwera kwakukulu, pofika abale ndi kuchita umboni za choonadi chako, monga umayenda m'choonadi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Pakuti ndinakondwera kwakukulu, pofika abale ndi kuchita umboni za choonadi chako, monga umayenda m'choonadi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Ine ndidaakondwa kwambiri pamene abale ena adafika nkumafotokoza za moyo wako m'choona, ndiponso za m'mene umayendera motsata choona. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Ine ndinali ndi chimwemwe chachikulu pamene abale ena anafika nʼkundifotokozera za kukhulupirika kwako pa choonadi ndiponso mmene umayendera motsata choonadi. Onani mutuwo |