3 Yohane 1:4 - Buku Lopatulika4 Ndilibe chimwemwe choposa ichi, chakuti ndimva za ana anga kuti alikuyenda m'choonadi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndilibe chimwemwe choposa ichi, chakuti ndimva za ana anga kuti alikuyenda m'choonadi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Palibe chondikondweretsa kwambiri koposa kumva kuti ana anga akuyenda m'choona. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Palibe chondikondweretsa kwambiri kuposa kumva kuti ana anga akukhala mʼchoonadi. Onani mutuwo |