3 Yohane 1:4 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Palibe chondikondweretsa kwambiri kuposa kumva kuti ana anga akukhala mʼchoonadi. Onani mutuwoBuku Lopatulika4 Ndilibe chimwemwe choposa ichi, chakuti ndimva za ana anga kuti alikuyenda m'choonadi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndilibe chimwemwe choposa ichi, chakuti ndimva za ana anga kuti alikuyenda m'choonadi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Palibe chondikondweretsa kwambiri koposa kumva kuti ana anga akuyenda m'choona. Onani mutuwo |
Solomoni anayankha kuti, “Inu munaonetsa kukoma mtima kwanu kwakukulu kwa kapolo wanu, abambo anga Davide, chifukwa anali wokhulupirika pamaso panu, wolungama mtima ndiponso wa mtima wangwiro. Inu mukupitirizabe kukoma mtima kwanu kwakukulu kwa iye ndipo mwamupatsa mwana kuti akhale pa mpando wake waufumu lero lino.