2 Samueli 7:5 - Buku Lopatulika5 Kauze mtumiki wanga Davide, kuti, Atero Yehova, Kodi iwe udzandimangira nyumba yakuti ndikhalemo Ine? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Kauze mtumiki wanga Davide, kuti, Atero Yehova, Kodi iwe udzandimangira nyumba yakuti ndikhalemo Ine? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 “Kamuuze mtumiki wanga Davide kuti Ine Chauta ndikuti, Kani wayesa udzandimangira ndiwe nyumba yoti ndizikhalamo? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 “Pita kamuwuze mtumiki wanga Davide kuti, ‘Yehova akunena kuti: kodi ndiwe amene udzandimangira Ine nyumba yokhalamo? Onani mutuwo |