Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Samueli 7:4 - Buku Lopatulika

4 Ndipo kunali usiku womwewo mau a Yehova anafika kwa Natani, kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ndipo kunali usiku womwewo mau a Yehova anafika kwa Natani, kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Koma usiku womwewo Chauta adauza Natani kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Usiku umenewo mawu a Yehova anafika kwa Natani ndipo anati,

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 7:4
7 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova anatumiza Natani kwa Davide. Ndipo anafika kwa iye nanena naye, Mu mzinda wina munali anthu awiri; wina wolemera, wina wosauka.


Ndipo Natani anati kwa mfumuyo, Mukani muchite chonse chili mumtima mwanu, pakuti Yehova ali nanu.


Kauze mtumiki wanga Davide, kuti, Atero Yehova, Kodi iwe udzandimangira nyumba yakuti ndikhalemo Ine?


Kuyambira tsiku lakutulutsa Ine anthu anga Aisraele m'dziko la Ejipito, sindinasankhe mzinda uliwonse mwa mafuko onse a Israele kumangamo nyumba yokhalamo dzina langa, koma ndinasankha Davide kukhala mfumu ya anthu anga Aisraele.


Ndipo usiku womwewo mau a Mulungu anadzera Natani, ndi kuti,


Pakuti Ambuye Yehova sadzachita kanthu osawulula chinsinsi chake kwa atumiki ake aneneri.


Ndipo anati, Tamvani, tsono mau anga; pakakhala mneneri pakati pa inu, Ine Yehova ndidzizindikiritsa kwa iye m'masomphenya, ndinena naye m'kulota.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa