Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Samueli 7:4 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Usiku umenewo mawu a Yehova anafika kwa Natani ndipo anati,

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

4 Ndipo kunali usiku womwewo mau a Yehova anafika kwa Natani, kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ndipo kunali usiku womwewo mau a Yehova anafika kwa Natani, kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Koma usiku womwewo Chauta adauza Natani kuti,

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 7:4
7 Mawu Ofanana  

Tsono Yehova anatumiza Natani kwa Davide. Atafika kwa Davide anati, “Panali anthu awiri mʼmizinda ina, wina wolemera ndi wina wosauka.


Natani anayankha mfumu kuti, “Chitani chilichonse chimene chili mu mtima mwanu chifukwa Yehova ali nanu.”


“Pita kamuwuze mtumiki wanga Davide kuti, ‘Yehova akunena kuti: kodi ndiwe amene udzandimangira Ine nyumba yokhalamo?


‘Kuyambira tsiku limene ndinatulutsa anthu anga Aisraeli ku Igupto, sindinasankhe mzinda wina uliwonse pa fuko lina lililonse la Aisraeli kuti kumeneko andimangire Nyumba, koma ndasankha Davide kuti alamulire anthu anga Aisraeli.’


Usiku umenewo mawu a Mulungu anafika kwa Natani, ndipo anati,


Zoonadi Ambuye Yehova sachita kanthu asanawulule zimene akufuna kuchita kwa atumiki ake, aneneri.


Mulungu anati, “Mverani mawu anga: “Pakakhala mneneri wa Yehova pakati panu, ndimadzionetsera kwa iyeyo mʼmasomphenya, ndimayankhula naye mʼmaloto.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa