2 Samueli 7:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo Natani anati kwa mfumuyo, Mukani muchite chonse chili mumtima mwanu, pakuti Yehova ali nanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo Natani anati kwa mfumuyo, Mukani muchite chonse chili mumtima mwanu, pakuti Yehova ali nanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Natani adauza mfumu kuti, “Ai, chitani chilichonse chimene mukuganiza mumtima mwanu, poti Chauta ali nanu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Natani anayankha mfumu kuti, “Chitani chilichonse chimene chili mu mtima mwanu chifukwa Yehova ali nanu.” Onani mutuwo |