2 Samueli 7:6 - Buku Lopatulika6 Pakuti sindinakhale m'nyumba kuyambira tsiku lija ndinatulutsa ana a Israele ku Ejipito kufikira lero lomwe, koma ndinayenda m'chihema ndi m'nyumba wamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Pakuti sindinakhala m'nyumba kuyambira tsiku lija ndinatulutsa ana a Israele ku Ejipito kufikira lero lomwe, koma ndinayenda m'chihema ndi m'nyumba wamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ine sindidakhalepo m'nyumba chiyambire tsiku limene ndidatulutsa Aisraele ku Ejipito mpaka lero lino. Ndakhala ndikuyenda uku ndi uku ndipo mokhala mwanga munali m'hema. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Ine sindinakhalepo mʼnyumba kuyambira tsiku limene ndinatulutsa Aisraeli mʼdziko la Igupto mpaka lero lino. Ndakhala ndikuyenda uku ndi uku ndipo mokhala mwanga munali mu tenti. Onani mutuwo |