Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Samueli 24:8 - Buku Lopatulika

8 Chomwecho pamene atayenda dziko lonse anafika ku Yerusalemu pakutha miyezi isanu ndi inai, ndi masiku makumi awiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Chomwecho pamene atayenda dziko lonse anafika ku Yerusalemu pakutha miyezi isanu ndi inai, ndi masiku makumi awiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Motero, atabzola dziko lonselo, adadzafika ku Yerusalemu itatha miyezi isanu ndi inai ndi masiku makumi aŵiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Atayendayenda mʼdziko lonse anabwerera ku Yerusalemu patapita miyezi isanu ndi inayi ndi masiku makumi awiri.

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 24:8
2 Mawu Ofanana  

nafika ku linga la Tiro ndi kumizinda yonse ya Ahivi ndi ya Akanani; natulukira kumwera kwa Yuda ku Beereseba.


Ndipo Yowabu anapereka kwa mfumu kuchuluka kwa anthu adawawerenga; ndipo mu Israele munali anthu zikwi mazana asanu ndi atatu, ngwazi zosolola lupanga; ndi anthu a Yuda ndiwo zikwi mazana asanu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa