2 Samueli 22:51 - Buku Lopatulika51 Iye apatsa mfumu yake chipulumutso chachikulu; naonetsera chifundo wodzozedwa wake, kwa Davide ndi mbeu yake ku nthawi zonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201451 Iye apatsa mfumu yake chipulumutso chachikulu; naonetsera chifundo wodzozedwa wake, kwa Davide ndi mbeu yake ku nthawi zonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa51 Mulungu amathandiza mfumu yake kuti izipambana nthaŵi ndi nthaŵi. Amaonetsa chikondi chake chosasinthika kwa wodzozedwa wake, ndiye kuti kwa Davide ndi kwa zidzukulu zake mpaka muyaya.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero51 “Iye amapereka chipambano chachikulu kwa mfumu yake, amaonetsa kukoma mtima kwa wodzozedwa wake, kwa Davide ndi zidzukulu zake kwamuyaya.” Onani mutuwo |