2 Samueli 22:50 - Buku Lopatulika50 Chifukwa chake ndidzakuongani Yehova, pakati pa amitundu, ndipo ndidzaimba zolemekeza dzina lanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201450 Chifukwa chake ndidzakuongani Yehova, pakati pa amitundu, ndipo ndidzaimba zolemekeza dzina lanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa50 “Chifukwa cha zimenezi ndidzakuyamikani Inu Chauta, pakati pa mitundu ya anthu, ndidzaimba nyimbo zotamanda dzina lanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero50 Choncho ine ndidzakutamandani Inu Yehova, pakati pa anthu a mitundu ina; ndidzayimba nyimbo zotamanda dzina lanu. Onani mutuwo |