2 Samueli 22:49 - Buku Lopatulika49 Amene anditulutsa kwa adani anga; inde mundikweza ine pamwamba pa iwo akundiukira; mundipulumutsa kwa munthu wachiwawa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201449 Amene anditulutsa kwa adani anga; inde mundikweza ine pamwamba pa iwo akundiukira; mundipulumutsa kwa munthu wachiwawa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa49 Ndinu amene mudandipulumutsa kwa adani anga. Mudandikweza pamwamba pa ondiwukira, mudandilanditsa kwa anthu ankhanza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero49 amene amandimasula mʼmanja mwa adani anga. Inu munandikuza kuposa adani anga; munandilanditsa mʼmanja mwa anthu ankhanza. Onani mutuwo |