2 Samueli 22:44 - Buku Lopatulika44 Inunso munandipulumutsa ine pa kulimbana kwa anthu anga; munandisunga ndikhale mutu wa amitundu; Anthu amene sindinawadziwe adzanditumikira ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201444 Inunso munandipulumutsa ine pa kulimbana kwa anthu anga; munandisunga ndikhale mutu wa amitundu; Anthu amene sindinawadziwa adzanditumikira ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa44 “Mudandipulumutsa kwa anthu anga ondiwukira. Mudandisunga kuti ndikhale wolamulira mitundu yonse. Choncho anthu osaŵadziŵa adayamba kunditumikira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero44 “Inu mwandipulumutsa mʼmanja mwa mitundu ya anthu; Inu mwandisunga kuti ndikhale mtsogoleri wa anthu a mitundu ina. Anthu amene sindikuwadziwa ali pansi pa ulamuliro wanga. Onani mutuwo |