2 Samueli 22:35 - Buku Lopatulika35 Iye aphunzitsa manja anga nkhondo; kotero kuti manja anga alifula uta wamkuwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201435 Iye aphunzitsa manja anga nkhondo; kotero kuti manja anga alifula uta wamkuwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa35 Amaphunzitsa manja anga kamenyedwe ka nkhondo, kotero kuti ndingathe kupinda uta wachitsulo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero35 Iye amaphunzitsa manja anga kuchita nkhondo; manja anga amatha kuthyola uta wachitsulo. Onani mutuwo |