2 Samueli 22:34 - Buku Lopatulika34 Iye asandutsa mapazi ake akunga mapazi a mbawala; nandiika pa misanje yanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Iye asandutsa mapazi ake akunga mapazi a mbawala; nandiika pa misanje yanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Amalimbitsa mapazi anga ngati a mbaŵala, ndipo amandisunga bwino ku mapiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Iye amasandutsa mapazi anga kukhala ngati ambawala yayikazi; Iye amandithandiza kuyimirira pamwamba pa mapiri. Onani mutuwo |