Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Samueli 22:30 - Buku Lopatulika

30 Pakuti ndi Inu ndithamangira gulu; ndi Mulungu wanga ndilumphira linga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 Pakuti ndi Inu ndithamangira gulu; ndi Mulungu wanga ndilumphira linga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Ndi chithandizo chanu ndingathe kugonjetsa gulu la ankhondo. Ndi chithangato chanu, Inu Mulungu, ndingathe kupambana.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 Ndi thandizo lanu nditha kulimbana ndi gulu la ankhondo, ndi Mulungu wanga nditha kuchita zosatheka ndi munthu.

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 22:30
6 Mawu Ofanana  

Kunena za Mulungu, njira yake ili yangwiro; mau a Yehova anayesedwa; Iye ndiye chikopa kwa onse akukhulupirira Iye.


Ndipo mfumu ndi anthu ake anamuka ku Yerusalemu kuyambana nao Ayebusi, nzika za dziko; ndiwo ananena kwa Davide ndi kuti, Sudzalowa muno, koma akhungu ndi opunduka adzakupirikitsa; ndiko kunena kuti, Davide sangathe kulowa muno.


Pakuti mwa Inu ndipyola khamu la anthu; ndipo mwa Mulungu wanga ndilumphira linga.


Koma m'zonsezi, ife tilakatu, mwa Iye amene anatikonda.


Ndikhoza zonse mwa Iye wondipatsa mphamvuyo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa