2 Samueli 22:29 - Buku Lopatulika29 Pakuti Inu ndinu nyali yanga, Yehova; ndipo Yehova adzaunika mumdima mwanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Pakuti Inu ndinu nyali yanga, Yehova; ndipo Yehova adzaunika mumdima mwanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Ndithu Inu Chauta, ndinu nyale yanga, Inu Mulungu, mumandiwunikira mu mdima. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Inu Yehova, ndinu nyale yanga; Yehova wasandutsa mdima wanga kukhala kuwunika. Onani mutuwo |