2 Samueli 22:28 - Buku Lopatulika28 Ndipo mudzapulumutsa anthu osautsidwa; koma maso anu ali pa odzikuza kuti muwachepetse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Ndipo mudzapulumutsa anthu osautsidwa; koma maso anu ali pa odzikuza kuti muwachepetse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Paja anthu odzichepetsa Inu mumaŵapulumutsa, koma anthu odzikuza mumaŵatsitsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Inu mumapulumutsa anthu odzichepetsa, koma maso anu amatsutsana ndi odzikuza ndipo mumawatsitsa. Onani mutuwo |