Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Samueli 22:26 - Buku Lopatulika

26 Ndi chifundo Inu mudzadzionetsa wachifundo, ndi munthu wangwiro mudzadzionetsa wangwiro.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

26 Ndi chifundo Inu mudzadzionetsa wachifundo, ndi munthu wangwiro mudzadzionetsa wangwiro.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

26 “Kwa anthu okhulupirika, Inu Mulungu mumadziwonetsa okhulupirika, kwa anthu aungwiro mumadziwonetsa abwino kotheratu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

26 “Kwa wokhulupirika, Inu mumaonetsa kukhulupirika kwanu, kwa anthu amakhalidwe abwino, Inu mumaonetsanso makhalidwe abwino,

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 22:26
3 Mawu Ofanana  

Ndi oyera mtima mudzadzionetsa woyera mtima; ndi otsutsatsutsa mudzadzionetsa wopotoza.


Odala ali akuchitira chifundo; chifukwa adzalandira chifundo.


Pakuti chiweruziro chilibe chifundo kwa iye amene sanachite chifundo; chifundo chidzitamandira kutsutsana nacho chiweruziro.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa