2 Samueli 22:21 - Buku Lopatulika21 Yehova anandibwezera monga mwa cholungama changa; monga mwa kuyera kwa manja anga anandipatsa mphotho. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Yehova anandibwezera monga mwa cholungama changa; monga mwa kuyera kwa manja anga anandipatsa mphotho. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 “Chauta adandipatsa mphotho molingana ndi kulungama kwanga, adandifupa molingana ndi ungwiro wanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 “Yehova wandithandiza molingana ndi chilungamo changa; molingana ndi makhalidwe anga abwino, Iye wandipulumutsa. Onani mutuwo |