2 Samueli 22:20 - Buku Lopatulika20 Iye ananditulutsanso ku malo aakulu; Iye anandipulumutsa, chifukwa akondwera ndi ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Iye ananditulutsanso ku malo akulu; Iye anandipulumutsa, chifukwa akondwera ndi ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Adakandifikitsa ku malo amtendere, adandipulumutsa chifukwa adakondwera nane. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Iye anandipititsa kumalo otakasuka; anandipulumutsa chifukwa amakondwera nane. Onani mutuwo |