Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Samueli 13:16 - Buku Lopatulika

16 Koma iye ananena naye, Usamatero, pakuti choipa ichi chakuti ulikundipirikitsa nchachikulu choposa china chija unandichitira ine. Koma anakana kumvera.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Koma iye ananena naye, Usamatero, pakuti choipa ichi chakuti ulikundipirikitsa nchachikulu choposa china chija unandichitira ine. Koma anakana kumvera.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Koma Tamarayo adati, “Iyai, mlongo wanga, kundipirikitsa chotere nkulakwa koposa zimene wandichitazi.” Koma Aminoni sadafune kumva zimene ankanena Tamarazo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Iye anayankha, “Ayi! Kundithamangitsa kukhala kulakwa kwakukulu kuposa zimene wachita kale kwa ine.” Koma anakana kumumvera.

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 13:16
2 Mawu Ofanana  

Atatero Aminoni anadana naye ndi chidani chachikulu kopambana; pakuti chidani chimene anamuda nacho, chinali chachikulu koposa chikondi adamkonda nacho. Ndipo Aminoni ananena naye, Nyamuka, choka.


Pomwepo anaitana mnyamata wake amene anamtumikira, nati, Tulutsa mkazi uyu kwa ine, nupiringidze chitseko atapita iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa