Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Samueli 13:15 - Buku Lopatulika

15 Atatero Aminoni anadana naye ndi chidani chachikulu kopambana; pakuti chidani chimene anamuda nacho, chinali chachikulu koposa chikondi adamkonda nacho. Ndipo Aminoni ananena naye, Nyamuka, choka.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Atatero Aminoni anadana naye ndi chidani chachikulu kopambana; pakuti chidani chimene anamuda nacho, chinali chachikulu koposa chikondi adamkonda nacho. Ndipo Aminoni ananena naye, Nyamuka, choka.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Pambuyo pake Aminoni adayamba kudana naye kwabasi Tamarayo, kotero kuti chidani chake ndi Tamara chidakula kwambiri kuposa chikondi chimene adaamkonda nacho. Ndipo Aminoniyo adauza Tamara kuti, “Dzuka, kazipita.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Atatero Amnoni anadana naye kwambiri. Iyeyo anamuda kuposa momwe anamukondera. Amnoni anati, “Dzuka ndipo tuluka!”

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 13:15
3 Mawu Ofanana  

Koma iye sadafune kumvera mau ake, ndipo popeza anali wamphamvu ndi iye, anamkakamiza, nagona naye.


Koma iye ananena naye, Usamatero, pakuti choipa ichi chakuti ulikundipirikitsa nchachikulu choposa china chija unandichitira ine. Koma anakana kumvera.


Namdzera a ku Babiloni ku kama wa chikondi, namdetsa ndi chigololo chao, iyenso anadetsedwa nao; atatero moyo wake unafukidwa nao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa