2 Samueli 13:14 - Buku Lopatulika14 Koma iye sadafune kumvera mau ake, ndipo popeza anali wamphamvu ndi iye, anamkakamiza, nagona naye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Koma iye sadafuna kumvera mau ake, ndipo popeza anali wamphamvu ndi iye, anamkakamiza, nagona naye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Koma Aminoni sadamve zimene ankanena Tamarazo. Ndipo popeza kuti anali ndi mphamvu zoposa Tamara, Aminoniyo adamkakamiza Tamarayo nagona naye. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Koma sanamvere zimene amanena Tamara ndipo popeza anali wamphamvu kuposa Tamarayo, iye anamugwirira. Onani mutuwo |