2 Samueli 12:5 - Buku Lopatulika5 Pamenepo mkwiyo wa Davide unayaka ndithu pa munthuyo, nati kwa Natani, Pali Yehova, munthu amene anachita ichi, ayenera kumupha; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Pamenepo mkwiyo wa Davide unayaka ndithu pa munthuyo, nati kwa Natani, Pali Yehova, munthu amene anachita ichi, ayenera kumupha; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Adauza Natani kuti, “Pali Chauta wamoyo, munthu amene adachita zimeneziyu, ayenera kuphedwa basi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Davide anapsa mtima kwambiri chifukwa cha munthuyo ndipo anati kwa Natani, “Pali Yehova, munthu amene anachita zimenezi ayenera kufa basi! Onani mutuwo |