2 Samueli 12:5 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Davide anapsa mtima kwambiri chifukwa cha munthuyo ndipo anati kwa Natani, “Pali Yehova, munthu amene anachita zimenezi ayenera kufa basi! Onani mutuwoBuku Lopatulika5 Pamenepo mkwiyo wa Davide unayaka ndithu pa munthuyo, nati kwa Natani, Pali Yehova, munthu amene anachita ichi, ayenera kumupha; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Pamenepo mkwiyo wa Davide unayaka ndithu pa munthuyo, nati kwa Natani, Pali Yehova, munthu amene anachita ichi, ayenera kumupha; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Adauza Natani kuti, “Pali Chauta wamoyo, munthu amene adachita zimeneziyu, ayenera kuphedwa basi. Onani mutuwo |