2 Samueli 10:12 - Buku Lopatulika12 Ulimbike mtima, ndipo tichite chamuna lero chifukwa cha anthu athu ndi mizinda ya Mulungu wathu; Yehova nachite chomkomera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ulimbike mtima, ndipo tichite chamuna lero chifukwa cha anthu athu ndi midzi ya Mulungu wathu; Yehova nachite chomkomera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Limba mtima, ndipo tichite chamuna chifukwa cha anthu athu, ndiponso chifukwa cha mizinda ya Mulungu wathu. Chauta achite zimene zimkomere.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Limba mtima ndipo timenyane nawo mopanda mantha chifukwa cha anthu athu ndi mizinda ya Mulungu wathu. Yehova achite chomukomera pamaso pake.” Onani mutuwo |