2 Samueli 10:13 - Buku Lopatulika13 Chomwecho Yowabu ndi anthu amene anali naye anayandikira kuponyana nkhondo ndi Aaramu. Ndipo iwowa anathawa pamaso pake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Chomwecho Yowabu ndi anthu amene anali naye anayandikira kuponyana nkhondo ndi Aaramu. Ndipo iwowa anathawa pamaso pake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Choncho Yowabu ndi anthu ake adasendera pafupi ndi Asiriya aja kuti amenyane nawo nkhondo, koma Asiriyawo adathaŵa iye akufika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Choncho Yowabu ndi ankhondo amene anali naye anapita kukamenyana ndi Aaramu, ndipo iwo anathawa pamaso pake. Onani mutuwo |