2 Samueli 1:8 - Buku Lopatulika8 Nanena, Ndiwe yani? Ndipo ndinayankha kuti, Ndine Mwamaleke. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Nanena, Ndiwe yani? Ndipo ndinayankha kuti, Ndine Mwamaleke. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Adandifunsa kuti, ‘Ndiwe yani?’ Ine ndidati, ‘Ndine Mwamaleke.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Iye anandifunsa, “Iwe ndiwe yani?” Ine ndinayankha kuti, “Ndine Mwamaleki.” Onani mutuwo |