2 Samueli 1:8 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Iye anandifunsa, “Iwe ndiwe yani?” Ine ndinayankha kuti, “Ndine Mwamaleki.” Onani mutuwoBuku Lopatulika8 Nanena, Ndiwe yani? Ndipo ndinayankha kuti, Ndine Mwamaleke. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Nanena, Ndiwe yani? Ndipo ndinayankha kuti, Ndine Mwamaleke. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Adandifunsa kuti, ‘Ndiwe yani?’ Ine ndidati, ‘Ndine Mwamaleke.’ Onani mutuwo |