2 Samueli 1:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo iye pakucheukira m'mbuyo mwake anandiona, nandiitana. Ndipo ndinayankha, Ndine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo iye pakucheukira m'mbuyo mwake anandiona, nandiitana. Ndipo ndinayankha, Ndine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Tsono Saulo atacheuka nandiwona, adandiitana. Ndidavomera kuti, ‘Ŵaŵa.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Pamene anatembenuka ndi kundiona ine, iye anandiyitana, ndipo ndinati, ‘Kodi ndichite chiyani?’ ” Onani mutuwo |