1 Samueli 8:4 - Buku Lopatulika4 Pamenepo akulu onse a Israele anasonkhana, nadza kwa Samuele ku Rama; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Pamenepo akulu onse a Israele anasonkhana, nadza kwa Samuele ku Rama; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Tsono akuluakulu onse a Aisraele adasonkhana nadza kwa Samuele ku Rama. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Tsono akuluakulu onse a Israeli anasonkhana pamodzi ndipo anabwera kwa Samueli ku Rama. Onani mutuwo |