Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Samueli 8:4 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Tsono akuluakulu onse a Israeli anasonkhana pamodzi ndipo anabwera kwa Samueli ku Rama.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

4 Pamenepo akulu onse a Israele anasonkhana, nadza kwa Samuele ku Rama;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Pamenepo akulu onse a Israele anasonkhana, nadza kwa Samuele ku Rama;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Tsono akuluakulu onse a Aisraele adasonkhana nadza kwa Samuele ku Rama.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 8:4
8 Mawu Ofanana  

Abineri anakambirana ndi akuluakulu a Israeli ndipo anati, “Kwa kanthawi mwakhala mukufuna kulonga Davide kuti akhale mfumu yanu.


Akuluakulu onse a Israeli atafika kwa Mfumu Davide ku Hebroni, mfumu inachita nawo pangano ku Hebroni pamaso pa Yehova, ndipo anamudzoza Davide kukhala mfumu ya Israeli.


Ndipo Yehova anati kwa Mose, “Bwera ku phiri kuno kwa Yehova, iwe pamodzi ndi Aaroni, Nadabu, Abihu ndi akuluakulu a Israeli makumi asanu ndi awiri. Enanu mundipembedze muli chapatali.


“Pita, ukawasonkhanitse akuluakulu a Israeli ndipo ukati kwa iwo, ‘Yehova, Mulungu wa makolo anu, Mulungu wa Abrahamu, Isake ndi Yakobo, anandionekera ndipo akuti Iye wadzakuyenderani ndipo waona mmene Aigupto akukuzunzirani.


Elikana ndi banja lake anadzuka mmawa mwake nakapemphera pamaso pa Yehova. Pambuyo pake anabwerera kwawo ku Rama. Elikana anakhala pamodzi ndi mkazi wake, ndipo Yehova anamukumbuka Hanayo.


Akuluakulu a mzinda wa Yabesi anati kwa iye, “Utipatse masiku asanu ndi awiri kuti titumize uthenga mu Israeli monse. Ngati sipapezeka wodzatipulumutsa, ndiye ife tidzadzipereka kwa iwe.”


Koma pambuyo pake ankabwerera ku Rama, kumene kunali nyumba yake. Ankaweruza Aisraeli kumeneko. Ndipo iye anamanga guwa lansembe la Yehova kumeneko.


Samueli anawawuza anthu amene amamupempha mfumu aja mawu onse a Yehova.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa