Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 8:2 - Buku Lopatulika

2 Dzina la mwana wake woyamba ndiye Yowele, ndi dzina la wachiwiri ndiye Abiya; ndiwo oweruza a ku Beereseba.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Dzina la mwana wake woyamba ndiye Yowele, ndi dzina la wachiwiri ndiye Abiya; ndiwo oweruza a ku Beereseba.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Mwana wake wachisamba anali Yowele, wachiŵiri anali Abiya. Iwoŵa ankaweruza ku Beereseba.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Mwana wake woyamba anali Yoweli, wachiwiri anali Abiya, ndipo ankaweruza ku Beeriseba.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 8:2
7 Mawu Ofanana  

Ndipo Abrahamu anabwera kwa anyamata ake, ndipo anauka nayenda pamodzi kumuka ku Beereseba; ndipo anakhala Abrahamu pa Beereseba.


Ndipo Israele anamuka ulendo wake ndi zonse anali nazo, nafika ku Beereseba, napereka nsembe kwa Mulungu wa Isaki atate wake.


Ndipo iye ataona chimenechi, ananyamuka, nathawa kupulumutsa moyo, nafika ku Beereseba wa ku Yuda, nasiya mnyamata wake pamenepo.


ndi Salumu anabala Hilikiya, ndi Hilikiya anabala Azariya,


Ndi ana a Samuele: woyamba Yowele, ndi wachiwiri Abiya.


mwana wa Izihara, mwana wa Kohati, mwana wa Levi, mwana wa Israele.


koma musamafuna Betele, kapena kumalowa mu Giligala; musamapita ku Beereseba; pakuti Giligala adzalowadi m'ndende, ndi Betele adzasanduka chabe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa