1 Samueli 8:2 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Mwana wake woyamba anali Yoweli, wachiwiri anali Abiya, ndipo ankaweruza ku Beeriseba. Onani mutuwoBuku Lopatulika2 Dzina la mwana wake woyamba ndiye Yowele, ndi dzina la wachiwiri ndiye Abiya; ndiwo oweruza a ku Beereseba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Dzina la mwana wake woyamba ndiye Yowele, ndi dzina la wachiwiri ndiye Abiya; ndiwo oweruza a ku Beereseba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Mwana wake wachisamba anali Yowele, wachiŵiri anali Abiya. Iwoŵa ankaweruza ku Beereseba. Onani mutuwo |