1 Samueli 31:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo Afilisti anapirikitsa, osawaleka Saulo ndi ana ake; ndipo Afilisti anapha Yonatani, ndi Abinadabu, ndi Malikisuwa, ana a Saulo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo Afilisti anapirikitsa, osawaleka Saulo ndi ana ake; ndipo Afilisti anapha Yonatani, ndi Abinadabu, ndi Malikisuwa, ana a Saulo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Afilistiwo adalondola Saulo ndi ana ake, ndipo adapha Yonatani, Abinadabu ndi Malikusuwa, ana a Saulo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Afilisti anapanikiza kwambiri Sauli ndi ana ake, ndipo anapha Yonatani, Abinadabu ndi Maliki-Suwa. Onani mutuwo |