1 Samueli 31:11 - Buku Lopatulika11 Koma pamene a ku Yabesi-Giliyadi anamva zimene Afilisti anamchitira Saulo, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Koma pamene a ku Yabesi-Giliyadi anamva zimene Afilisti anamchitira Saulo, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Koma anthu a ku Yabesi-Giliyadi atamva zimene Afilisti adaamchita Saulo, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Pamene anthu a ku Yabesi Giliyadi anamva zimene Afilisti anachitira Sauli, Onani mutuwo |