Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 31:11 - Buku Lopatulika

11 Koma pamene a ku Yabesi-Giliyadi anamva zimene Afilisti anamchitira Saulo,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Koma pamene a ku Yabesi-Giliyadi anamva zimene Afilisti anamchitira Saulo,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Koma anthu a ku Yabesi-Giliyadi atamva zimene Afilisti adaamchita Saulo,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Pamene anthu a ku Yabesi Giliyadi anamva zimene Afilisti anachitira Sauli,

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 31:11
5 Mawu Ofanana  

Ndipo anthu Ayuda anabwera namdzoza Davide pomwepo akhale mfumu ya nyumba ya Yuda. Ndipo wina anauza Davide kuti, Anthu a ku Yabesi-Giliyadi ndiwo amene anamuika Saulo.


Ndipo Davide ananka natenga mafupa a Saulo ndi mafupa a Yonatani mwana wake kwa anthu a ku Yabesi-Giliyadi amene anawaba m'khwalala la Beteseani, kumene Afilisti adawapachika, tsiku lija Afilistiwo anapha Saulo ku Gilibowa;


Ndipo onse a Yabesi-Giliyadi, atamva zonse Afilisti adachitira Saulo,


Nati iwo, Kodi pali lina la mafuko a Israele losakwera kudza kwa Yehova ku Mizipa? Ndipo taonani, kuchokera ku Yabesi-Giliyadi sanadze mmodzi kumisasa, kumsonkhano.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa