1 Samueli 27:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo Davide anakhala ndi Akisi ku Gati, iye ndi anthu ake, munthu yense ndi a pabanja pake, inde Davide ndi akazi ake awiri, Ahinowamu wa ku Yezireele, ndi Abigaile wa ku Karimele, mkazi wa Nabala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo Davide anakhala ndi Akisi ku Gati, iye ndi anthu ake, munthu yense ndi a pabanja pake, inde Davide ndi akazi ake awiri, Ahinowamu wa ku Yezireele, ndi Abigaile wa ku Karimele, mkazi wa Nabala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Adakhala ndi Akisi ku Gati, iyeyo pamodzi ndi anthu ake, aliyense ndi banja lake. Davide anali ndi akazi ake aŵiri, Ahinowamu wa ku Yezireele ndi Abigaile wa ku Karimele, mkazi wamasiye wa Nabala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Davide anakhala ndi Akisi ku Gati pamodzi ndi ankhondo ake, aliyense ndi banja lake. Davide ali ndi akazi ake awiri, Ahinoamu wa ku Yezireeli ndi Abigayeli wa ku Karimeli, mkazi wamasiye wa Nabala. Onani mutuwo |