1 Samueli 27:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo anauza Saulo kuti Davide anathawira ku Gati; ndipo iye sanamfunenso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo anauza Saulo kuti Davide anathawira ku Gati; ndipo iye sanamfunenso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Saulo atamva kuti Davide wathaŵira ku Gati, sadamfunefunenso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Sauli anamva kuti Davide wathawira ku Gati, ndipo sanamufunefunenso. Onani mutuwo |